Article
M'zimayi amene wadzuka mu bokosi, akufuna kumukwilira. Umu ndi mmene zakhalira

M'zimayi amene wadzuka mu bokosi, akufuna kumukwilira. Umu ndi mmene zakhalira

M'zimayi amene anafa wadzuka mu bokosi, akufuna kumukwilira.

Mayiyu amene ndi wa dzaka 88 zakubadwa, anasala pang'ono kuti amuike mmanda pamene anazizimuka. Izi zadabwitsa anthu ambili ku dziko la Czech Republic ndipo vuto lalikulu akuti anali akuchipatala amene analengeza kuti mayiyu wamwalira koma asanamulabadile bwinobwino.

Amuna wo a mayiwa akuti zonse zi zinayamba pamene anadzuka mamawa ndikuona kuti akazawo sakupeza bwino, koma atafika ku chipatala anangofikila kuwauuza kuti akazawo amwalira ngakhale a chipatala wo sanachite nawo chidwi kwenikweni.

Mpaka kukafika kosambisa maliro osadziwabe kuti munthu ali moyo, kufikila kuika thupi lawo mu bokosi ndi pamene amazizimuka (ma bokosi omwe amatsegula nkhope kumaoneka aja)

Apolisi tikunena pano ayambapo kafukufuku kwa ogwila ntchito ku chipatala chi pokanika kupeleka chisamaliro choyenela komanso pogwila ntchito mosazipeleka, akuti ndikutheka anthu ambili amatha ku walengeza kuti amwalira koma ali moyo ndiye ndi koyenela kupanga po kanthu.

Tikunena pano mayiyo ali ku chipatala chomwecho ndipo a kulandilano thandizo, ndipo ma report akuonetsa kuti akhala di bwino ndithu.

Zovuta, zinakakhala ku Malawi bwenzi patalowa kale zikhulupiliro apa.

Source of news: the daily mail

Admin Jeffrey

Comment Below

40 Comments

wizidowiladi@gmail.com

Zosachitilaso mwina umkuva kaitaneni azamba🤣🤣🤣🤣🤣

Dann January

Kunoko kumalawi nde kut mayiwo ndi mfiti 🤣🤣🤣

Bright botha

Uyu Basitu wapulumuka

Travis DaWRLD🌍

Ku Malawi ukhala ufiti😭😂😂😂

Nkalo Igwee Amos Bwanali

Kunakakhala ku Malawi kuno akanangomalizitsa sure 🙌

Hope

Mmmm zovuta kwambiri

Shahidah Keisha Louis

Kuli Ku Ku Africa kuno akanawakong'ontha kuwamalidxitsa

Mary samangaya

Zovutat kobasi

Chrispine maxwell

Zimachitika

Pearson waya

Ambiri amafelad m'bokosi akakwililidwa

Symon mafupa

We are protected to God

Eston k

It's not yet for her

Charity

Nthawi yake sinakwane,

Milliam chabvunga

Nthawi yoti afe sinakwane alimbikile kupemphera

Milliam chabvunga

Nthawi yoti afe sinakwane alimbikile kupemphera

Vegah

Ndipo ku Malawi sitizatheka

Irvine

Eeh achipatala pulizi

Keith 24

Sometimes people they are die but God sent them back to repent. Sure

Precious Davison

Achipatala masiku ano akumanyada kwambir akumakhala ngat sazamwalira

Reshy

Zonvuta mmmh

Kay cee Øbhebha

Achipatala pena matiyikitsa a2 amoyo2 🙄

Happy

Zovutatu mmhu

argentina banda

Kuli khmalawi uva ndi ufiti🤣🤣🤣🤣🤣🤣

Chiwawula

Zimachitika

Monique

Yangadyedatu pele

James Kawinga Phililimon

Zosakhala bwino 🤔🤔🤔

Chicco

Zosakhala bwino

Sam Chiphaka

Izi si zachilendo.

Flano

Eeèeee iyiyi kma ndiyina yake

Ellery make

Nkhan ngat izizi ndizovuta kuweluza kwake, nanga mpaka kukasambisa munthu osazuka kukadzuka nthawi yoona nkhope, let God judge

Jack Murera

Zosakhala bwino😥 atadyatu angapotu awa mkumat athelako pomwe zisali chomcho

Ethel kaunda

Tsiku lawo laifa silinakwane,Allah alinawo cholinga

Dixon mponda

Zovuta 😌

F-one

Zovutatu

Patrick kachere

Anachita bwino kuzuka mwa changu adakangochedwa pang'ono bwez atadzukira Ali Pasi mkufa imfa yowawa

Géññàh Sydé Mw

Zinthu zake🙌

Esther Bwanali

Moyo unazaza ndi zinyengo ,,, nthawi yake sinakwane Mulunguysanafune🙏🙏

Mathews brown

A Chipatala akatero adali busy pa tiktok

Justice winicco

Yemwe ananena kuti mayiwo amwalira koma osamulabadira akuyenera kukayakha mlandu.

Luka Thamanga

A police akuyenera kupeleka chirango kwa munthu amene adalengeza kuti mayiyu wamwalira kuti anzake opanga zotelewa atendelepo mphunziro.

upload your music with us to get maximum reach out!