Agwa pansi ndikukomoka atamva kuti Mkazi wake wabereka ana 5
Bambo wina dzina lake Adamu Muhammed adagwa pansi atamva kuti mkazi wake wabereka ana 5 pakamodzi
Malingana ndi anthu omwe anali pamalowa nthawi yomwe bamboyu amauzidwa uthenga wabwino kuti mkazi wake wabereka ana 5 bamboyu adagwa ndipo ogwira ntchito m’chipatalachi adathamangira kumuthandiza ndipo adakwanitsa kumudzutsa
Bamboyu atasisimuka anayankhura motere
“Zikomo Mulungu chifukwa cha Mphatso ya ana yomwe mwandipatsa koma ndikulephera kumvetsa.
Sindinadziwe kuti tikuyembekezera mapasa 5 Tsopano, tilibe chuma kapena ndalama zokwanira kulipira m’chipatala, komanso kusamalira ana atatu nthawi imodzi” bamboyu anatero uku misodzi ikutuluka
Iye anafotokozaso kuti iyeyu budget yokonzekera inali ya mwana modzi osati mpaka 5 pakamodzi ayi
Anthu omwe anali pomwepo adatsimikizira kuti kubadwa kwa ana kunayenda bwino, koma banjalo likufunika thandizo la mankhwala, zakudya, ndi ndalama posachedwa kuti lisamalire ana.
“Banja limeneli likufunika thandizo mokuti Tikupempha boma ma NGO, magulu achipembedzo, ndi anthu ena okoma mtima kuti athandize” akubanja anatero
Nkhaniyi yachitika ku Nigeria Muli inu mungatani?
Ndingapangeso bwanj koposa kuthokoza?mulungu sangasokoneze olo pang'ono
God's plan always sungavetse
Kufela2
China chilichonse chimene mulungu a atipatsa amakhala Ali ndi cholinga komaso mulungu amatiyesa pofuna kutiona ku khulupilila kwathu mulungu amakhala ndi cholinga pa chilichonse
God bless you
Muzomse yamikani yehova, Ali ndi cholinga powapasa ana omsewo,
Pena mablessing akachuluka zimatheka kufainta ndithu
Mmmmm mkanachita zomwezo coz sizimene ndimaembekezera
It's a blessing from God, let's accept the situation no matter how, but God's name cannot be ashamed, He already made ways on how the family and the new comers will live and survive, we specially thank God for the protection to the mother, because since she conceived, eeish she has been in a tough condition, and giving birth to 5 at once and then all are alive it's not easy, praise God, I pray that the family should lack nothing
Chimudalitso Cha mulungu osazachiphweketsa 🎉😍🙌🙏
Zabwino kwabasi
Blessed family
Mphaso iyi yaposera maganizo athu mene timaganizira
Akamati chimdalitso mchimenechitu kkkkkk azabeleke chocho achina uje ulemera aja akhoza kusangalalatu
Kungoyamika kumwamba basi zonse kumusiyira Ambuye osadandaulaso zamavuto.Adabwa mkomwe kuchokere thandizo anthu aliko achikondi
Kkkkkk
Ok