Article
Zifukwa zodabwisa zomwe a Mussa asiyila kubereka ana ena

Zifukwa zodabwisa zomwe a Mussa asiyila kubereka ana ena

Bambo wina wa ku Uganda emwe ali ndi ana okwana 102 ndi zidzukulu 568 basi waganiza kuti asiile pompo kubeleka

A Musa omwe ali ndi zaka zakubadwa zokwana 70 tsopano awuza akazi awo onse 12 kuti ndi nthawi yoti apume ndikubereka ana atsopano ngakhale kuti nyonga zawo sikuti zathera pa ana 102 po ayi Koma pazifukwa zomwe iwowo azifotokoza Kulibwino asiile kaye pompo kufikira zifukwazo atazikonza atha kumazapitiliza kutsogoloku

Tisanakambe zifukwa zomwe a Musa awuzira azikazi awo kuti aime kaye kubereka tikambeko history Pangโ€™ono ya a Mussa

Iwowa akuti dzina lawo lakubadwa ndi Mussa Hasahya Kasera ochokera ku Uganda, Butaleja District Ndipo khumbo lawo lakhala lozakwanilisa Malemba a Bible โ€œBelekanani ngati Mchengaโ€ Ndipo zonsezi zinayambira Ndi Mkazi wawo oyamba amene anaberekelana naye ana okwana 15 Koma ataona kuti mphamvu zawo zikuchulukabe anakwatiraso wina kenakoso wina, kenakoso wina Mpaka kukwana Akazi 12

Tsopano nkhani yaikulu apa ndiyoti ndichifukwa chani a Mussa aganiza kuti achite break khwee! kukhalabe ndi ana ena anyuwani kuonjezera pa 102 omwe ali nawo kale?

Malingana ndi a Musa iwo afotokoza kuti kale kale anali ndizochita zogwirika Ndipo zimawayendera amakwanitsa kudyesa mabanja onse 12 koma pano chifukwa cha kukwera kwa zinthu komanso kusowa kwa ntchito Komanso ma business awo anasiya kuyenda ngati kale Ndichifukwa aganiza kuti ayambe ayima kubereka ana kuti kangachepe komwe ali nako akwanitsebe kusamalira ana 102 ndi zidzukulu 578 zomwe padakali pano ali nazo

A Musa anenesa kuti iwo nyonga adakali nazobe Koma mavuto a kusowa kwa ndalama ndiomwe awabwenza mbuyo kuti apange chiganizo choti awuze akazi awo onse 12 kuti ayambe ayima kaye kubereka ana atsopano

Admin Jeffrey

Comment Below

29 Comments

Jay moscow mw artist

Greet madala

Pemphero ballon

Aaaa aonetsa zisuzo

Haswel

Madala aiwonela kutali sakwanisa kudyesa

Precious Oscar c chakwana

Adawa amasatirad bible

New phoebe

Eewee komatu ntchito aigwira abambo awa ichiiii

Topolapalipose

Ofunika makosana muvaye mukangowapanga sapot system ๐Ÿ˜

Munthu ND yemwey mussah

Munthu ND yemwey mussah

Victor gabliel

Owoo? Zina ukamva

Ireen kaunga

Mbaka ana 102

Eliphaz Caseby Banda

Solomoniology

Joyce kambwera

Nzovuta kwambiri and sindikuvesabe ...mpaka akazi 12 ayi Zikomo

Luka Thamanga

Anthu kunjakutu akupakula beansness osati zibwana๐Ÿ™„๐Ÿ™„๐Ÿ™„

Ignatius kampanje

Despite kukwanilitsa malemba komano pa zaka zawo iwowo akufunika angosiya basi nanga azichita kupikisana ndi ana awo kubeleka

Slapsy

Nde akundiuza kut anawo samagwira ntchito kuzithandiza okha coz akuoneka ndakulutu mpaka zizukulu

Gibo lanje

Ndalama alinazo.opanda kanthu sangakwanitse zimenezi

Imran Cassim

Mphanvu bas

Kkkkk Koma yaaa mpaka 102 mmm

Kkkkk Koma voto anawo sangapuzile

Elizabeth Jere

Eeee koma yaaa ndee Ali ndi mphamvu

Jonathan Fungulani

Money talks .

James Harrison

Koma yah ๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚, mukufuna kukwanirisa malemba et

Faithinah

Economy yake imene mpaka 102, ana amenewo palibe angaphunzile school

??

A Mussa kod ndnu sheikh??

Edda Omali

Apa nde malembo awakwanitsadi chifukwa 102 +578 eeeeeh ndi mzindatu

Madah mponda

Ulemu wawo a musa uku nde kukwanilitsa malemba

Bernard Ephraim

Mmmm koma ndiye mpaka 102 eee ameneyi amafunadi kukwanilitsa malemba

Ennalah phiri

Koma ndiye , enafe ana awiri akulephera kudyetsa

Ibrahim Gorge

Awa ndi makina opangira katundu wa boma

Letia Phiri

Koma ndie mulutu

Peter jailos

Ana 102 ๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚angakhale ndimudzitu uyu

upload your music with us to get maximum reach out!