Article
Kodi anthu a ku Burkina Faso akuti chani zakubanidwa kwa ma website olaula Dziko mwawo?

Kodi anthu a ku Burkina Faso akuti chani zakubanidwa kwa ma website olaula Dziko mwawo?

Chifukwa chimene President wa ku Burkina Faso wapangira Bun ma video ndi ma website olaula dziko mwake

Tsopano President Ibrahim Traore officially walengeza kuti Wapanga Bun porrrrn videos and websites dziko lawo la Burkina Faso

Izi zikutanthauza kuti ma citizen a ku Burkina Faso sazitha kapena kuti sizimatheka kupanga search ma website kuti aonere ma video akusaweruzika

Malingana ndi Ibrahim Traore akukhulupilira kuti ma website ndi ma videos akusaweruzika aja amasokoneza achinyamata kaganizidwe kazinthu mu zinthu zosiyanasiyana

Ibrahim Traore wati kale kale lija mwinako zinali zabwinobwino chifukwa ma phone kapena amapezeka ndi akuluakulu okha okha koma pano kubwera kwa Technology ndi ana omwe akumakhala ndi phone adakali achichepere kwambiri kotero pena ukangoyasa data pa phone pakopo olo usanapange search koma pamabwera zithunzi zovula zimene amakhala ma advertiser achita kuziikapo mwadala ndipo iye wati zinthu ngati izi sizoona kuti ana aziziona zili ngati kuphwanya ufulu wawo komanso kulowesa pansi culture yathu ya ma africans

Traore anapitilizaso kunena kuti malo moti wachinyamata azikhala busy kuganiza zamoyo wake kuti angatukuleso bwanji dziko lake sizoona kuti azipanga spend more time on internet kuonera ma video akusaweruzika aja kotero tsopano iyeyu wachita bun ma website onse oterowo pofuna kuteteza maufulu a ana omwe akumagwiritsa ntchito internet adakali aong'ono pa zinthu zokhunza school osati zithuzi zovula kumangobwera pa phone pawo olo ngakhale asanapange search ngati mene zikumachitikira masiku ano

Komatu ngakhale izi zili choncho anthu ena mdziko la Burkina Faso sanasangalare ndichiganizo chimenechi pakuti akuti iwowo popanda ma video komanso ma website akusaweruzika sangakhale ndipo moyo wawo uzisowa kenakake

Inu maganizo anu ndi otani pa chiganizo Cha Traore chochotsa komanso kubana ma video ndi ma website akusaweruzika? Chitani comment timve kuti Kodi ku Malawi kuno mungafuneso zitatero?

Admin Jeffrey

Comment Below

135 Comments

Ndrama Zitali Zitali

That's the way to go..

Luka joh

Wachita bwino mavedio oluula siabwino kwa munthu wina aliyetse chifukwa ayabitsa chisebwere

Jimmy

That mn is my favorite

Ibrahima daud

Yes monga ngat one nde ndagwilidzana nae traole ndganidzo lozamali ndi I would like kut ife monga aMalawi tikanakhala nd apule onkhwima maganidzo ngat traole mmmm ine apaaaaaaa!! Dziko lanthu lija bwedz tikulimva kukoma heavy

Sandboy Da Bloodlinez ๐Ÿฉธ

Zingathe kuthandiza kwa achinyamata kuchepesapo mchitidwe ogwririra

Wama VPN

Nchifukwa kuli ma VPN

Machita1 Sydney

Ku Malawi ๐Ÿ‡ฒ๐Ÿ‡ผ kunoso akanabana tikanasangalalaso kwambiri

Mujaya Dailesi Special

Zitachitika kumalawi kuno zingakhale bwino kwambir chifukwa ngakhale kuno so Ana Ali ndimaphone ndpo zimenez zikuchitika...

Vumzy

Chifukwa chan anthu oterewa sali akuno kwathu kunali magufuli apa uyoso traore koma kuno maloza okha

Che-Bauleni

Kunonso apange bun

Lee Mornie

Amakwana koma. Zichitikenso kuno ku Malawi

Lee Mornie

Amakwana koma. Zichitikenso kuno ku Malawi

Lee Mornie

Amakwana koma. Zichitikenso kuno ku Malawi

David Mankhambo

The brotherhood is proud of you Ibrahim ,,,keep it up

Dorafa ART SIGNS

Mtsogoleri koma ameneyu

KING SLEY

That's a nice move TRA, indeed porrrn videos lead to downfall of African culture.

Innocent chomveka

Ngati kuli president yemwe akufunila zabwino anthu ake ,ndiye ndi Traole,akuona kufunikila kolemekeza ufulu wa ana mdziko mwake.Ndichifukwa chake tikaonetsetsa mdziko la Bukina Fanso zinthu zikuyenda bwino kamba kautsogoleri wamasomphenya.Kwaiwo omwe akuti sangakhale opanda mavideo akusayeluzikawo,akadakonda akadzifufuza kuti kodi kwa iwo vuto ndichani.

G. Louis

I like Traore wise guy and God fearing man. God why not Malawi ๐Ÿ’”๐Ÿ’”๐Ÿ–ค

Emmanuel chapepa

True definition of a leader who lead by example

Dizzo bwoy Sparta

Chiganiza chabwino chimenechi sakunama ayi coz zimachotsaso uzimu

Girafeezo hohsah

Wachita bwino sanalkwise

Dalitso issah

Nice decision amuna traore

Mboba

Traore uja simunthu wamba ndipo that decision akulu ndiyabwino koopsa but us people canโ€™t see that.....

Rayyan

Mashalllah ๐Ÿ˜˜๐Ÿ˜˜๐Ÿ˜˜

Rodney minika

Thank you for recognizing for that opportunity to add my comment here in this box , inshort Ibrahim Traore has it good , and if this can proceed here in malawi it can as well help the reduce of bad behavior of indulging on early sexuals and reduce of deaths caused by young โค๏ธ broken of under aged boys and girls ( teens)

Gerald

Zili

HARXCENTEE

Idea is concrete...I like it ..I wish ku Malawi kunakakhala choncho coz many youths are being taken down mentally coz of pornography and musterbation.

Ackras M Mbewe

Chiganizo chokoma kwabasi chimene President Yu wapanga m'dziko mwake. Moti ngakhareso kuno ku Malawi kuno ndi zokomaso ndithu, zitakharaso kuti zachitika motero momwemo kupanga burn. Chifukwa zinthu izi zili ndi cholinga chofuna kulimbana ndi moyo wa uzimu kuti usamapite chitsogolo mu miyoyo ya anthu. Ndiyeno chifukwa ca ichi zingakhareso bwino kuletsa ku burner kuno ku Malawi.

alubi assan

ndipo or atachotsa lero miyoyo yathu itha kusitha kwambri. pa phone titha kumakghala busy ndi zithu za phindu monga ma business kupanga ma practice zithu zosiyana siya. pamene ma porn ndi zithu zomwe zikulepheletsa athu kupita patsogolo ndo internet. chitsanzo ineyo almost my life panopa ndimadalira internet kuti didye koma 2 munits ina yake ndimazasiya za business ndikuyamba kupanga zoonera zimenezo chifukwa cha advert yeni yeni.

Thafy anthonie

Ineyo ndikuona kut Traore ndi president ofunila zabwino dziko lake komaso ali ndi chikhumbokhumbo chodzafuna anthu ake komaso iyeyo onse adzalowe kumtendere wamulungu

Rabson

Yah ndimaganizo anzeru kwambiri Ndipo tili pambuyo pake

Yusufu

Waganiza bwino kwambir ndipo mulungu azimudalitsa

Fred Lemon

It's a gud development

Joxy cee

President wanzeru kwambili

Hendrix

smart decision...

Dah rheku

Bun

Thews G

Ndipo sanalakwise zimenezi zumalimbikisa chiwelewele kwambili Pano kukwelana kunaphweka chifukwa anthu akumayenda Ali ndi zibaba kale Kuzela pakuonera ma video asagaduzowa

Felix jimu

Kwathu kuno Bora zikanatero mwna kukharako mw wasogoro labwno

Blessings sale

Ndi president oganiza ndie ameneyu,ndi zoona achinyamata akutaya nthawi kuonera zopusa,ifenso zitatelo zingathandize kwambir

Lordgaga Nkhoma

Yah zilibwino chifukwa zimatisokonezadi achinyamata mix panopa or ma ads akabwera amakhala atsikana ovula zimene munthu zimakupatsa attractive kuwonera porn ndikumabunyura zimene zili tchimo pamaso pa Mulungu ndiye kunoso ku Malawi atapanga block zikhoza kukhala bhow pat

Chief Odogu Onyekwa

Maganizo abwino kwambiri ndipo maiko akwathu kuno Ku Africa akanachita ngati mene wachitira Ibrahim bwenzi zili bwino koopsa

Rafick Fort

President traore waganiza bwino kwambiri

Sulaymana Waya

Wachita bwino sanalakwise

Mike

Kunena fact zinthu zija olo kunoso atachotsa palibe vuto coz zimapanga drain mindset ya achinyamata timakanika kuganiza zolongosoka

Genias

Ndipo kwambili kunoso zchtike

Alfred Power from Lilongwe, Malingunde.

Kupanga bun ma websites ama porn, ndi chinthu chabwino chifukwa ana ambiri masiku ano akumayamba zogonana akadali achichepere kwambiri nkumatenga mimba zomwe zikupangisaso kuti azisiyira school panjira nkukalowa ku mabanja ali ang'ono kwambiri. Wachinyamata ameneyu sangatukule dziko lake ayi. Nzofunika ndipo nzabwino ngati Malawi itatsatila chiganizo chimenechi. Zikomo

Wishes

Izi zilibwino Kwambili end ndi chiganizo chabwino

Kiah chy jere

traore tsadalakwitse fkwa akufna kukonza zne otsat kuwononga zn2 ngat m'mene zkuchtkir nziko la2 lino

Alex Banda

Great idea Mr President mkanakonda kunoso akanachita zomwezi๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚ ndili paselipa

Hassan Hamis

Uyuyu ndi msilamu weni weni And We need this kind of leadership in our country

Ismaila Allie Yassin

It It seems that Traore is a very good president, especially when it comes to making decisions. This decision is good and will help reduce prostitution in the country.

Ishmael

Maganizo abwino kwambir

Godfrey

It's a good decision and I proud of him, technology must have some measurements like this so that our youth can concentrate other good things not just wasting time for stupid things

Bliss

That's gud I dear brw

Miove kanola

Wichita boh

John mwakyanjala

Yeah โ˜บ๏ธ I do agree with him

Maxy chakomaliza

Izi ndiziona ndipo ine ndikugwilisana nazo cz kt muon pano ana ambili analowelera cz anayamba kuziona ali achichepele izi zikufunikaso kumalawi kuno pano Mwana wazaka 15 akumakhala ndi Mwana mzake chifukwa chazimenezi chiganizoo chabwino kwambili

Big ~G

Eya wachita bwino...

Suleiman

Ndipo kwambili that's why dziko lathu likupita patsi chifukwa chakuganiza popelewela komwe azisogoleli anthu Ali Nako thawi yayitali ikumathela pa ma porn chomcho angaganize zithu zotukula Malawi??

OMEX P JULY

He is a wise b4 becames presidential state , i support the genius idea he rare things abroad indeed that kind of behave he does is very scarcity in africa , may humble God continues bless his ideas ๐Ÿค˜๐Ÿ”ฅ๐Ÿ™

Zex

Traore is a hero end he know how to hand the world ,coz this website is disturbing more children and more youths ,for example the increasing of rape one of the cause it's porn

Chrispine Muzungu

this is the example of a living president am supporting it โœ…โœ…๐Ÿ”ฅ

Gerbuzar

๐Ÿ˜‚๐Ÿ˜‚sangakhare nd mogo?

Chimwemwe Blanket

It is a good decision and ndukusapota mfundo imeneo

SOSTEN CHRIFORD

Eya wakhoza I wish tikadapangaso tero

Isaac asima

Adha aja ndi genius idont bฤบame him for every decision he makes

William chiweche

Apanga bwino kwambilitu achinyamata akubunyura kwambiri

Ahmad Salim

Yes that is good desertion to the country Ndipo ku Malawi kunonso zikanatelo zikanakhala bwino kwambili

Fortunete

Ayi samalakwitsa wapanga bwino kwambil zimaonengaso Ka ganizidwe kwa ana zimenezo coz amat tikaesele uona zot mpaka atenga nazo mimba

Gracious

This is great movement, God is with him Traole๐Ÿ‘Œ

Wachisena Mlhomwe

Yap. Maganizo abwino kwambir. Ndngakondwenso zitatero kathy kuno

Davie

Ndi dolo kangapo ameneyo kunonso I wish atapangaso burn ndthu

Dah Gang

Kod ma president athu kuno Ku Malawi sangayesele kukopela izi??? This guy is a genius ๐Ÿ˜Ž

Abdul-rasheed Salika

Ineyo to say the fact; mfundo iyiyi 106% ndugwirizana nayo kwabasi ndithu, coz iyayi anthuwa akumaonjeza kwabasi sizoonayi izi

Oliver

The decision is as massive as Gold. We don't need porn in Africa. Young men spend much of their time watching nonsense on internent and getting no penny in return. The one who posted it gets a lot of coins but the one watching it gets nothing, what's that game?! We need young people who can think of how to have their social lives developed, not being addicted to foolish things like ponos, big up Traore, one day the whole Africa will bun intetnent and be like the 1800s, just to redeem the young generation. I believe that will happen one day.

Alkalk nthikira

Uyu nde president oganizila komaso odziwa ubwino ndi kuipa kwa zinthu zina pa ma citizens ake...

Anko-Sho

He is a leader, leading a better future for the kids who will be the future leaders

Osborn Yesaya

Well done Mr president, ndipo ndi zinthu zonyasa kumene kumaona zinthu zolaula congratulations Mr president

Shaib me

Apapa ngati zingapitilire,dziko la burkina faso likhalanso la anthu okhulupilira Mulungu kwambiri,long live Ibrahim, Kumalawi mwina titapereka mwai kwa bwana TULI atha kuchitako pang'ono

Jay sparrow25

Apap nxen waith aaa zimatisokonez kwambir aaa

Ethel

Chilungamo ukupweteka akhalitse ameneyu

Tobious Original Mawanja

President uyu ndi oganiza kwambiri komanso zikuonetseratu kuti akudziwa mavuto amoyo wa munthu mma levels onse, NDI pemphero langa kuti Ambuye atichotsere chitsiru tili nacho ifechi ndikutipatsa munthu oganiza mwakuya ngati president Traore

vibray mvula

izizi ndzimene zkufunikaso ku mkalawi kuno kodi tkukanikiranji kudzuka ngati traore?

Emmanuel Kalipeni

Zinthu zabwino kwambiri

Faith

President of the world, he deserve the chair ๐Ÿซก

John mwamphashi

Nanga zabwino zipose apaaaa waitha Traore

Tsanzo Dickson

Ukuku nde kuganiza bho coz azungu aja aapanga ma video akusaweluzika ndicholinga chofuna kutichedwesa, kma apapa mayuthi ambiri ku Burkina Faso ๐Ÿ‡ง๐Ÿ‡ซ akhala busy nd zinthu ziti ziziwapindulira...i wish Traole akanakhala wathuwathu ku Malawi ๐Ÿ‡ฒ๐Ÿ‡ผ kuno

Ishmael jazeelu

Aaaaaa anthu amene akutsutsana ndi zimenezo akulamulidwa ndi ziwanda kumalawi kuno adakatero zinakatichitila ubwino ๐Ÿ‘

Emdash

Ndi nzeru komamaso umunthu

Bhinghi Man

Waitha koma kaya Malawi ikukhalira pati kaya

King Dove

Apa tipanga ndalama. Tiziwagulisa ma citizens aku Burkina Faso wo through WhatsApp or Email. Tipha makwacha

Fadem

Walakwisa ibrahim coz ma porn ndi feel komaso njira imoz yopewer sex ngt sukufuna kumana ndi nkaz umango streamer ma porn nkuzthandza wekha

Tim Cee Masiye

That's good idea

Aprilkingz-sly

Wise decision๐Ÿ’ฏ

JASCOW

Akhalise Ibrahim traore ife ma African timaziwika bwino ndi chikhalodwe ndye nzofunika kusunga chikhalidwecho God bless Ibrahim traore forever and ever

Mestard mbambo

Perfect

battry

asadandaule tiziwatumizila pa wap

Peckson

fixing the country in good way.. mindset change first

Blessings Chakhwantha

Traole has done a very remarkable job to his citizens. Pornographic clips destroy minds. If I had time to speak to him I would also advise him to ban gambling, both physical and online gambling ( aviator) eeshi mchipembedzoso icho

Ghazza

Zofunika kom izi

Doba Arts medias solutions

Traore to the world smart guy all over world

Kapyola

This president is genius. I wish nkanakhala Burkinabe

PDee chiopyezo

๐ŸŒฌ๏ธKUNOooo!!!๐Ÿ’จ Tasangalala namuza ndinetu

Wise

Kopangira ban kuno kulibe????

Laston Musisi

Kunonso apange bun ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ

Innocent

Ichichi!!! Chipweteka ma presedent azake chikuganiza mwa nyo!!!!!!

Elder gisoz

Tipange WhatsApp group ndiziwagulisa anao

Bremeck mw

Ndipo Traore akhalitse ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ

ร˜ptรฏรฑรฑรนm Hรธrrฤรฑ

I think this guy he's more careful on his kind cause being a reader you have to take risks and don't expect all the pple to love you but it takes an ignorant person so see this as a burden but truth to be told shout out to Ibrahim

Nicholas Mwale

Uyu nd dolo uyu

Oscar

Uyuyu akanakhala kuti Sali pa banja kanapasa sister wanga Bwezi inu mukunditcha mulamu wake wa Traore

Osman Alick

I think this president indeed wants good things for his people, especially youths coz exposing pornographies to youth affects them both mentally and physically. I wish if our president here in Malawi copy that style

Kacmu balaka

Ichichi ndi chiganizo chabwino, chifukwa sikwabwino kumaonera zinthu zomwe zitha kukusokomeza ubongo, kuno kwathu zitatero zingakhale bwino kwambiri, komamso ana ambiri amakhala osalemekeza makolo chifukwa CHOTI amakhala akuwadziwa mmene alili

KONDWANI KANDIERO

Wachita bwino.chifukwa izi zithandiza kuti, achinyamata akhale ndi nthawi yotukula dziko lawo. komanso kuphunzira zinthu zomwe zingawanthandize pa moyo wawo, pamene akugwilitsa makina a Internet.

Shaffie

Apa ndpomwe ndaona kt traore yu ndi dolo kangapo

Wattie

Wachitabwino kwambiri chison ndichakut kwathu kuno sanapange olo mpang'ono pomwe

Junior trinity phiri

Maganizo abwino kwambiri

Sings

Wachita bwino

Brian

Amen

Charles

Achita bwino, Zidzenso kuno zimenezo

Delior

Sanayiphonye wachita bho kwambili kunoso achose

Famous

Koma uyuyu Nd shasha

Praise

Chiganizo chabwino kwambiri

Chiwawula

Eya achita bwino kutero

Chancy

Wachita bwino

Van shuxy mw

Achita bwino cos achinyamata ambilife imatipweteka ndi peer pressure kuno kumalawi zitatero zitha kuchita bwinoso

ALIBU A SAIZI

Achita bwino kwambiri

Francis bendulo

Dziko lose lapas titakhala ndi anthu ngt awawa zinthu zintha kumayenda bwino kwambiri zed wachita bwino kwambiri

Cleverton Mbizi

Just good and perfect idea though some will fund alternative to find them despite being bun on the internet for them. This will just reduce availability of the videos which will reduce exposure to many individuals. Watching while young just induces youths to think that sex is the best thing ever they can plan of hence in their development plan they mix with sexual plans which leads to reduction in the performance of development plans for them. Mapanga awiri avumbwisa

Mathews Julius

Good ideas ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ๐Ÿ”ฅ

SUYA KIDDO

Izizi zokomera tili ndakazi ambilife koma zitabwera kuno ndili gulu lozikana sure ๐Ÿคง๐Ÿ˜ฃ

Thandi

I think wachita bho kwambiri,,staff ija ngakhale Kwa munthu wankulu imasokoneza kaganizidwe,, alesenso online gambling.

Lixy mw

Dolo

Osama dd

Gud decision ๐Ÿ‘ MashAllah traore

Dann January

Uyu ndi shasha wenwen

upload your music with us to get maximum reach out!