Oimba wa ku Nigeria Burna Boy walonjeza kuti amupatsa ndalama President wa ku Burkina Faso
Tisanaifotokoze nkhani yonse Funso mkumati Koma izizi ndizoonadi oimba mpaka angafike size yopanga challenge kuti apereka ndalama kwa President wa dziko? Kodi kapena yawo ija ma artist ma stunt?
Tiyambe ndi mtengo omwe Burna Boy ama charger per show, Malingana ndi kafukufuku emwe ali pa internet ndiwoti Oimba wa ku Nigeria yu kuti akaimbe ku show yako amalipilisa ndalama zokwana 1 Million US Dollars komanso kupatula pamenepo umayenera kuti umulipilire private Jet yochoka kwao kukafika komwe kuli show zimene ndalama zonse ukaziphatikiza zimakhala zambiri
So now let’s get to the bottom of the story, Pamene Maiko ambiri muno mu Africa akuyamikira ulamuliro wa President wa ku Burkina Faso Ibrahim Traore indedi ndizoona naye Burna Boy walilonjeza dzikolo kuti alipangira zinthu izi posafuna anything in return
Burna Boy walonjeza dziko la Burkina Faso kuti apitako kukapangitsa Concert kapena kuti Show yoti samulipira chilichonse ndipo ndalama yonse yomwe itakapangidwe ku Show imeneyi yonseyo azaipereka kwa President Ibrahim Traole kuti ithandizire kugwira ntchito za Chitukuko zomwe President yu akupanga kale Mdzikomo
Padakali pano Ibrahim Traore sanayankhurepo chilichonse pa nkhaniyi Koma Burna Boy ali ready Ndipo akuthokoza pa ulamuliro wa President Traore posintha kaganizidwe ka ma president ena ambiri muno mu Africa
Great
Mumatha
Thus great idea
Izo ndizofunikira potengera umunthu womwe burn boy alinawo 🙏🙏🙏🙏🙏
Apo ndiye titha kunena kuti Africa yabwela sopan
Eee kungot Ibrahim traore ndi president wodabwisa zochitika zake km khani iyi traore alola kt athandize potengera naye burna boy ndi waku africa 🌍 nde achita bwino akatelo
Nthawi yoti MA afilikazi agwirane manja ndiyiyi
Zosangalasa kumalimbikisana
It's okay, because the money he gonna gain in his show will benefit the country of Burkina Faso.thats great 👍
Burna Boy ndiDolo
Zlibwino heavy
Amakwana Burna
Burna boy cover🙏
Burna boy cover🙏
Akachoka kumeneko azakomaneso nd chakwera ku malawi kwanuko
Akachoka kumeneko azakomaneso nd chakwera ku malawi kwanuko
Akachoka kumeneko azakomaneso nd chakwera ku malawi kwanuko
Akachoka kumeneko azakomaneso nd chakwera ku malawi kwanuko
Akachoka kumeneko azakomaneso nd chakwera ku malawi kwanuko
Akachoka kumeneko azakomaneso nd chakwera ku malawi kwanuko
Bola asakhala kuti watumidwatu uyu
This president akufuna ndimuphe
Ok
So nice
Koma nde manthanyura akuyenda malondatu🤣🤣🤣
That's powerful
Let's appreciate what our fellow Africans are doing osamangosapota azunguyi
That's powerful every one needs gift
That's great everyone needs gift
I like this forum
Yàaah it's good, don't mind far
Burna ndi African gient
Amutuma akatero
Watumidwa
Watumidwa ndi trump uyu sure
Uyu nd dola athad kupeleka
Ibrahim traore he is a good leader
Nane Niluyenera Nipiteko Uku
Thank you for the support and help with your gift
Zilibhoo km asamutengele ku mtoso paja mati mkazi amadya Ibrahim trore nayeso burna boy amalowama
Nzeru
GREAT THINKING
Zili bho